< Danieli 6 >

1 Kunamukomera Dariyo kusankha akalonga 120 kuti alamulire mu ufumu wonse,
Svidje se Dariju te postavi nad carstvom sto i pedeset upravitelja da budu nad svijem carstvom;
2 ndikusankha nduna zazikulu zitatu kuti ziwayangʼanire ndipo imodzi mwa ndunazo anali Danieli. Akalongawo amayangʼaniridwa ndi nduna zazikuluzo kuti zinthu za mfumu zisawonongeke.
A nad njima tri starješine, od kojih jedan bješe Danilo, kojima æe upravitelji davati raèune da ne bi caru bilo štete.
3 Tsono Danieli anadzionetsa kuti akhoza kugwira ntchito bwino kopambana nduna zinzake chifukwa anali wanzeru kwambiri. Ndiye mfumu inaganiza zomuyika kuti akhale woyangʼanira ufumu wonse.
A taj Danilo nadvišivaše starješine i upravitelje, jer u njemu bješe velik duh i car mišljaše da ga postavi nad svijem carstvom svojim.
4 Chifukwa cha ichi, anzake ndi akalonga anayesa kupeza zifukwa zomutsutsira Danieli pa kayendetsedwe ka ntchito za dzikolo, koma sanapeze cholakwa chilichonse. Iwo sanapeze chinyengo mwa iye, chifukwa anali wokhulupirika ndipo sankachita chinyengo kapena kutayirira ntchito.
Tada starješine i upravitelji gledahu kako bi našli što da zabave Danilu radi carstva; ali ne mogahu naæi zabave ni pogrješke, jer bješe vjeran, i ne nalažaše se u njega pogrješke ni mane.
5 Pomaliza, anthu awa ananena kuti, “Sitidzapeza cholakwa chilichonse chomutsutsira Danieli kupatula chokhacho chimene chikhudza chipembedzo cha Mulungu wake.”
Tada rekoše oni ljudi: neæemo naæi na toga Danila ništa, ako ne naðemo što na nj radi zakona Boga njegova.
6 Choncho akalonga ndi nduna pamodzi anapita kwa mfumu ndipo anati: “Inu mfumu Dariyo, mukhale ndi moyo wautali!
Tada doðoše starješine i upravitelji k caru, i rekoše mu ovako: Darije care, da si živ dovijeka.
7 Nduna zoyendetsa ufumu wanu, aphungu, akalonga ndi abwanamkubwa tonse tagwirizana kuti inu mfumu mukhazikitse lamulo ndi kulisindikiza kuti aliyense amene apemphera kwa mulungu wina kapena kwa munthu kupatula kwa inu mfumu, pa masiku makumi atatu otsatirawa, adzaponyedwa mʼdzenje la mikango.
Sve starješine u carstvu, poglavari i upravitelji, vijeænici i vojvode dogovoriše se da se postavi carska naredba i oštra zabrana da ko bi se god zamolio za što kome god bogu ili èovjeku za trideset dana osim tebi, care, da se baci u jamu lavovsku.
8 Tsopano inu mfumu khazikitsani lamulo limeneli ndipo musindikizepo dzina lanu kuti lisasinthike monga mwa malamulo a Amedi ndi Aperezi, amene sasinthidwa.”
Zato, care, postavi tu zabranu i napiši da se ne može promijeniti, po zakonu Midskom i Persijskom, koji je nepromjenit.
9 Choncho mfumu Dariyo anasindikizapo dzina lake pa lamuloli.
I car Darije napisa knjigu i zabranu.
10 Danieli atamva kuti lamulo lasindikizidwa, anapita ku nyumba kwake nalowa mʼchipinda chapamwamba chimene mazenera ake anali otsekula kuloza ku Yerusalemu. Katatu pa tsiku iye ankagwada pansi pa mawondo ndipo amapemphera, kuyamika Mulungu wake, monga momwe ankachitira kale.
A Danilo kad dozna da je knjiga napisana, otide svojoj kuæi, gdje bijahu otvoreni prozori u njegovoj sobi prema Jerusalimu, i padaše na koljena svoja tri puta na dan i moljaše se i hvalu davaše Bogu svojemu kao što èinjaše prije.
11 Ndipo anthu awa anapita pamodzi ndi kukapeza Danieli akupemphera ndi kupempha Mulungu wake kuti amuthandize.
Tada se sabraše oni ljudi, i naðoše Danila gdje se moli i pripada Bogu svojemu.
12 Kotero iwo anapita kwa mfumu ndipo anayankhula naye za lamulo lake kuti, “Kodi simunasindikize lamulo lakuti pa masiku makumi atatu otsatirawa aliyense amene apemphera kwa mulungu wina aliyense kapena kwa munthu kupatula kwa inu mfumu, adzaponyedwa mʼdzenje la mikango?” Mfumu inayankha kuti, “Lamulo lilipobe monga mwa malamulo a Amedi ndi Aperezi, amene sangathe kusinthika.”
I otidoše te rekoše caru za carsku zabranu: nijesi li napisao zapovijest, da ko bi se god zamolio kome god bogu ili èovjeku za trideset dana, osim tebi, care, da se baci u jamu lavovsku? Car odgovori i reèe: tako je po zakonu Midskom i Persijskom, koji je nepromjenit.
13 Kenaka iwo anati kwa mfumu, “Danieli, amene ndi mmodzi mwa akapolo ochokera ku Yuda, sakulabadira inu mfumu, kapena lamulo limene munasindikizapo dzina lanu lija. Iye akupempherabe katatu pa tsiku.”
Tada odgovoriše i rekoše caru: Danilo, koji je izmeðu roblja Judina, ne haje za te, care, ni za zabranu koju si napisao, nego se moli tri puta na dan svojom molitvom.
14 Mfumu itamva izi, inavutika kwambiri mu mtima mwake. Iyo inayesa kupeza njira yopulumutsira Danieli. Iyo inachita chotheka chilichonse kufikira kulowa kwa dzuwa kuti imupulumutse.
Tada car èuvši to ožalosti se vrlo, i naumi da izbavi Danila, i truðaše se do zahoda sunèanoga da ga izbavi.
15 Ndipo anthuwo anapita pamodzi kwa mfumu ndipo anati kwa iye, “Kumbukirani, inu mfumu kuti monga mwa lamulo la Amedi ndi Aperezi, palibe chimene mfumu inalamulira kapena kukhazikitsa chimasinthidwa.”
Tada oni ljudi sabraše se kod cara i rekoše caru: znaj, care, da je zakon u Midijana i Persijana da se nikakva zabrana i naredba, koju postavi car, ne mijenja.
16 Choncho mfumu inalamula, ndipo anabwera naye Danieli ndi kukamuponya mʼdzenje la mikango. Mfumu inati kwa Danieli, “Mulungu wako amene umutumikira nthawi zonse, akupulumutse!”
Tada car reèe te dovedoše Danila i baciše ga u jamu lavovsku; i car progovori i reèe Danilu: Bog tvoj, kojemu bez prestanka služiš, neka te izbavi.
17 Anatenga mwala natseka pa khoma pa dzenje la mikango, ndipo mfumu inadindapo chizindikiro chake ndi cha nduna zake kuti wina asasinthepo kanthu pa za Danieli.
I donesoše kamen i metnuše jami na vrata, i car ga zapeèati svojim prstenom i prstenom svojih knezova da se ništa ne promijeni za Danila.
18 Kenaka mfumu inabwerera ku nyumba yake ndipo inakhala usiku wonse osadya kanthu, osalola chosangalatsa chilichonse. Ndipo sinagone tulo.
Tada otide car u svoj dvor, i prenoæi ne jedavši niti dopustivši da mu se donese što èim bi se razveselio, i ne može zaspati.
19 Mʼbandakucha, mfumu inanyamuka ndi kufulumira kupita ku dzenje la mikango lija.
Potom car usta ujutru rano i otide brže k jami lavovskoj.
20 Itayandikira pa dzenjelo, inayitana Danieli moonetsa nkhawa, “Danieli, mtumiki wa Mulungu wa moyo! Kodi Mulungu wako, amene umutumikira nthawi zonse, wakulanditsa ku mikango?”
I kad doðe k jami, viknu Danila žalosnijem glasom; i progovori car i reèe Danilu: Danilo, slugo Boga živoga, Bog tvoj, kojemu služiš bez prestanka, može li te izbaviti od lavova?
21 Danieli anayankha kuti, “Inu mfumu mukhale ndi moyo wautali!
Tada Danilo reèe caru: care, da si živ dovijeka!
22 Mulungu wanga anatumiza mngelo wake, ndipo anatseka pakamwa pa mikango. Iyo sinandivulaze chifukwa Mulungu anaona kuti ndine wosalakwa ndi kutinso sindinakulakwireni inu mfumu.”
Bog moj posla anðela svojega i zatvori usta lavovima, te mi ne naudiše; jer se naðoh èist pred njim, a ni tebi, care, ne uèinih zla.
23 Mfumu inali ndi chimwemwe chopambana ndipo inalamulira kuti amutulutse Danieli mʼdzenjemo. Ndipo atamutulutsa Danieli mʼdzenjemo, sanapezeke ndi chilonda chilichonse pa thupi lake, chifukwa iye anadalira Mulungu wake.
Tada se car veoma obradova tomu, i zapovjedi da izvade Danila iz jame. I izvadiše Danila iz jame, i ne naðe se rane na njemu, jer vjerova Bogu svojemu.
24 Mwa lamulo la mfumu, anthu onse amene ananeneza Danieli aja anagwidwa ndi kukaponyedwa mʼdzenje la mikango, pamodzi ndi akazi awo ndi ana awo. Ndipo asanafike pansi pa dzenjelo, mikango inawawakha ndi mphamvu ndi kuteketa mafupa awo onse.
Potom zapovjedi car, te dovedoše ljude koji bijahu optužili Danila, i baciše u jamu lavovsku njih, djecu njihovu i žene njihove; i još ne doðoše na dno jami, a lavovi ih zgrabiše i sve im kosti potrše.
25 Kenaka mfumu Dariyo inalembera anthu a mitundu yonse, ndi anthu a ziyankhulo zosiyanasiyana a mʼdziko lonse kuti, “Mtendere uchuluke pakati panu!
Tada car Darije pisa svijem narodima i plemenima i jezicima što življahu u svoj zemlji: mir da vam se umnoži.
26 “Ndikukhazikitsa lamulo kuti paliponse mʼdziko langa anthu ayenera kuopa ndi kuchitira ulemu Mulungu wa Danieli.
Od mene je zapovijest da se u svoj državi carstva mojega svak boji i straši Boga Danilova, jer je on Bog živi, koji ostaje dovijeka, i carstvo se njegovo neæe rasuti, i vlast æe njegova biti do kraja;
27 Iye amalanditsa ndipo amapulumutsa,
On izbavlja i spasava, i èini znake i èudesa na nebu i na zemlji, on je izbavio Danila od sile lavovske.
28 Choncho Danieli anapeza ufulu pa nthawi ya ulamuliro wa Dariyo ndi ulamuliro wa Koresi wa ku Perisiya.
I taj Danilo bijaše sreæan za carovanja Darijeva i za carovanja Kira Persijanca.

< Danieli 6 >