< Amosi 5 >

1 Israeli, imva mawu awa, nyimbo ya maliro imene ndikuyimba za iweyo:
E HOOLOHE oukou i keia olelo, a'u e hapai aku nei no oukou, Oia hoi, he kanikau, e ka hale o ka Iseraela.
2 “Namwali Israeli wagwa, moti sadzadzukanso, wasiyidwa mʼdziko lake lomwe, popanda woti ndi kumudzutsa.”
Ua haule, aole e ala hou ae, ke kaikamahine puupaa o ka Iseraela: Ua kulaina oia maluna o kona aina iho: Aohe mea nana ia e hoala.
3 Ambuye Yehova akuti, “Mzinda umene udzapite ku nkhondo ndi anthu 1,000 amphamvu udzatsala ndi anthu 100 okha; mzinda umene udzapite ku nkhondo ndi anthu 100 amphamvu udzatsala ndi anthu khumi okha basi.”
No ka mea, ke olelo mai nei o Iehova ka Haku, peneia: O ko ke kulanakauhale i hele patausani aku, e koe mai no he haneri; A o ka mea i hele pahaneri aku, e koe mai no he umi, no ka hale o ka Iseraela.
4 Zimene Yehova akunena kwa nyumba ya Israeli ndi izi: “Mundifunefune kuti mukhale ndi moyo;
No ka mea, ke olelo mai nei o Iehova peneia i ka hale o ka Iseraela, E imi oukou ia'u, a e ola oukou.
5 musafunefune Beteli, musapite ku Giligala, musapite ku Beeriseba. Pakuti Giligala adzatengedwa ndithu kupita ku ukapolo, ndipo Beteli adzawonongekeratu.”
Aka, mai imi oukou i Betela, Aole hoi e komo i Gilegala, Aole e hele aku i Beereseba; No ka mea, he oiaio, e hele pio aku ko Gilegala, A e lilo o Betela i mea ole.
6 Funani Yehova kuti mukhale ndi moyo, mukapanda kutero Iye adzatentha nyumba ya Yosefe ngati moto; motowo udzawononga, ndipo sipadzakhala wina wozimitsa motowo ku Beteli.
E imi oukou ia Iehova, a e ola oukou; O lele mai ia, me he ahi la, ma ka hale o Iosepa, A e hoopau aku ia, Aohe mea nana ia e kinai ma Betela.
7 Inu amene mumasandutsa chiweruzo cholungama kukhala chowawa ndi kunyoza chilungamo.
E ka poe i hoolilo i ka olelo hoopono i mea awaawa, A hoolei i ka pono ma ka honua,
8 (Iye amene analenga nyenyezi za Nsangwe ndi Akamwiniatsatana, amene amasandutsa mdima kuti ukhale mmawa ndi kudetsa usana kuti ukhale usiku, amene amayitana madzi a mʼnyanja ndi kuwathira pa dziko lapansi, Yehova ndiye dzina lake.
E imi i ka mea nana i hana ia Peleiade a me Oriona, A hoolilo i ka malu o ka make i malamalama, A hoopouli i ke ao a lilo i po: Ka mea e hoopii ana i na wai o ka moana, A ninini iho ia lakou maluna o ka ili o ka honua: O Iehova kona inoa:
9 Iyeyo amabweretsa chiwonongeko modzidzimutsa pa anthu amphamvu ndi kuwononga mizinda yotetezedwa),
O ka mea e lawe mai i ka make maluna o ka poe ikaika, A e hoohiki mai i ka luku maluna o kahi paa.
10 inu mumadana ndi amene amadzudzula mʼbwalo la milandu ndi kunyoza amene amanena zoona.
Ke inaina nei lakou i ka mea e ao ana ma ka pukapa, A hoowahawaha lakou i ka mea e olelo pono ana.
11 Mumapondereza munthu wosauka ndi kumukakamiza kuti akupatseni tirigu. Nʼchifukwa chake, ngakhale mwamanga nyumba zamiyala yosema, inuyo simudzakhalamo. Ngakhale mwalima minda yabwino ya mphesa, inu simudzamwa vinyo wake.
No ia mea, no ko oukou hehi ana maluna o ka ilihune, A ke lawe nei oukou i ka ai makana mai ona aku la: Ua hana oukou i na hale pohaku i kalaiia, Aka, aole oukou e noho iloko o lakou; Ua kanu oukou i na pawaina maikai, Aka, aole oukou e inu i ka waina o lakou.
12 Pakuti Ine ndikudziwa kuchuluka kwa zolakwa zanu ndi kukula kwa machimo anu. Inu mumapondereza anthu olungama ndi kulandira ziphuphu ndipo anthu osauka simuwaweruza mwachilungamo mʼmabwalo anu amilandu.
No ka mea, ua ike au, he nui wale ko oukou lawehala ana, A me ko oukou mau hewa nui: E hoopilikia ana i ka poe hoopono, e lawe ana i ka uku kipe, A e hookahuli ana i ka pono o ka poe ilihune ma ka pukapa.
13 Nʼchifukwa chake pa nthawi yotere munthu wanzeru sayankhulapo kanthu, popeza ndi nthawi yoyipa.
No ia mea, e noho malie ka mea naauao i kela manawa; No ka mea, he manawa ino ia.
14 Muyike mtima wanu pa zabwino osati pa zoyipa, kuti mukhale ndi moyo. Mukatero Yehova Mulungu Wamphamvuzonse adzakhala nanu, monga mmene mumanenera kuti ali nanu.
E imi oukou i ka maikai, aole i ka hewa, i ola oukou; A pela e mau ai o Iehova, ke Akua o na kaua me oukou, e like me ka oukou i olelo ai.
15 Mudane ndi zoyipa, mukonde zabwino; mukhazikitse chiweruzo cholungama mʼmabwalo anu amilandu. Mwina mwake Yehova Mulungu Wamphamvuzonse adzachitira chifundo anthu otsala a mʼbanja la Yosefe.
E inaina i ka hewa, a e aloha i ka maikai, A e hookupaa oukou i ka hoopono ma ka pukapa: Malia paha e aloha mai o Iehova, ke Akua o na kaua, i ke koena o ka Iosepa.
16 Choncho izi ndi zimene Ambuye, Yehova Mulungu Wamphamvuzonse, akunena: “Mʼmisewu monse mudzakhala kulira mofuwula, ndi kulira chifukwa cha kuwawa kwa masautso kudzakhala paliponse. Adzayitana alimi kuti adzalire, ndipo anthu odziwa maliridwe anthetemya adzalira mofuwula.
No ia hoi, ke olelo mai nei o Iehova, ke Akua o na kaua, ka Haku, peneia; Ma na alanui a pau he auwe ana; A ma na wahi iwaho a pau, e olelo lakou, Auwe! auwe! A e kahea aku lakou i ka mea mahiai i ka u ana, A i ka poe ike e kanikau i ka uwe ana.
17 Mʼminda yonse ya mpesa mudzakhala kulira kokhakokha, pakuti Ine ndidzadutsa pakati panu,” akutero Yehova.
A ma na pawaina a pau ka uwe ana: No ka mea, e hele auanei au iwaena ou, wahi a Iehova.
18 Tsoka kwa inu amene mumalakalaka tsiku la Yehova! Chifukwa chiyani mumalakalaka tsiku la Yehova? Tsikulo kudzakhala mdima osati kuwala.
Auwe ka poe iini i ka la o Iehova! No ke aha la keia ia oukou? O ka la o Iehova, he pouli ia, aole he malamalama.
19 Lidzakhala ngati tsiku limene munthu pothawa mkango amakumana ndi chimbalangondo, ngati pamene munthu walowa mʼnyumba, natsamira dzanja lake pa khoma ndipo njoka nʼkuluma.
E like me ke kanaka i holo mai ke alo aku o ka liona, a halawai ka bea me ia: A i komo paha iloko o ka hale, a hilinai kona lima ma ka paia, a nahu mai ka nahesa ia ia.
20 Kodi tsiku la Yehova silidzakhala mdima osati kuwala, mdima wandiweyani, popanda powala pena paliponse?
Aole anei he pouli ka la o Iehova, me ka malamalama ole? A he pouli loa, aohe ona malamalama.
21 “Ndimadana nawo masiku anu achikondwerero ndipo ndimawanyoza; sindikondwera nayo misonkhano yanu.
Ke inaina nei au, ke hoowahawaha nei au i ko oukou mau ahaaina, Aole wau e oluolu i ko oukou mau halawai ana.
22 Ngakhale mupereke nsembe zopsereza ndi nsembe zachakudya, Ine sindidzazilandira. Ngakhale mupereke nsembe zabwino zachiyanjano, Ine sindidzaziyangʼana nʼkomwe.
Ina e kaumaha mai oukou no'u i ka oukou mau mohai kuni, a me ka oukou mau mohai makana, aole au e oluolu ia mea: Aole hoi au e manao i ka mohai aloha o ko oukou mau mea momona.
23 Musandisokose nazo nyimbo zanu! Sindidzamvetsera kulira kwa azeze anu.
E lawe ae oe mai o'u aku nei i ke oli ana o ka oukou mau mele; Aole au e hoolohe i ke kani ana o ko oukou mau viola.
24 Koma chiweruzo cholungama chiyende ngati madzi, chilungamo ngati mtsinje wosaphwa!
Aka, e hookaheia ka hoopono ana e like me ka wai, A o ka pono e like me ka waikahe ikaika.
25 “Kodi pa zaka makumi anayi zimene munakhala mʼchipululu muja munkandibweretsera nsembe ndi zopereka, inu nyumba ya Israeli?
Ua kaumaha mai anei oukou na'u i na mohai, a me na makana ma ka waonahele i na makahiki he kanaha, e ka hale o ka Iseraela?
26 Inu mwanyamula kachisi wa mfumu yanu, ndi nyenyezi ija Kaiwani, mulungu wanu, mafano amene munadzipangira.
Ua hali oukou i ka halelewa o ko oukou Moloka, A me ka hale o ko oukou mau kii, Ka hoku o ko oukou akua, ka mea a oukou i hana'i no oukou.
27 Nʼchifukwa chake Ine ndidzakupititsani ku ukapolo, kutali kupitirira ku Damasiko,” akutero Yehova, amene dzina lake ndi Mulungu Wamphamvuzonse.
Nolaila, e lawe pio aku au ia oukou ma o aku o Damaseko, wahi a Iehova, ke Akua o na kaua, kona inoa.

< Amosi 5 >