< 1 Mbiri 2 >

1 Ana a Israeli anali awa: Rubeni, Simeoni, Levi, Yuda, Isakara, Zebuloni,
Estos son los hijos de Israel: Rubén, Simeón, Leví, Judá, Isacar, Zabulón,
2 Dani, Yosefe, Benjamini, Nafutali, Gadi ndi Aseri.
Dan, José, Benjamín, Neftalí, Gad, y Aser.
3 Ana a Yuda anali awa: Eri, Onani ndi Sela. Ana atatu awa anabereka ndi mkazi wa Chikanaani, Batisuwa. Eri, mwana woyamba wa Yuda anali woyipa kwambiri pamaso pa Yehova, kotero Yehova anamupha.
Los hijos de Judá: Er, Onán, y Sela. Estos tres le nacieron de la hija de Súa, cananea. Y Er, primogénito de Judá, fue malo delante del SEÑOR; y lo mató.
4 Mpongozi wake Tamara anamuberekera Perezi ndi Zera. Ana onse a Yuda analipo asanu.
Y Tamar su nuera le dio a luz a Fares y a Zera; y así todos los hijos de Judá fueron cinco.
5 Ana a Perezi anali awa: Hezironi ndi Hamuli.
Los hijos de Fares: Hezrón y Hamul.
6 Ana a Zera anali awa: Zimuri, Etani, Hemani, Kalikoli ndi Dara. Onse analipo asanu.
Y los hijos de Zera: Zimri, Etán, Hemán, y Calcol, y Dara; en todos cinco.
7 Mwana wa Karimi anali Akani, amene anabweretsa mavuto pakati pa Israeli pamene anatenga zinthu zoyenera kuwonongedwa.
Hijo de Carmi fue Acán, el que alborotó a Israel, porque prevaricó en el anatema.
8 Mwana wa Etani anali Azariya.
Azarías fue hijo de Etán.
9 Ana amene anabadwa kwa Hezironi anali: Yerahimeeli, Ramu ndi Kelubai.
Los hijos que nacieron a Hezrón: Jerameel, Ram, y Quelubai.
10 Ramu anabereka Aminadabu ndipo Aminadabu anali abambo ake a Naasoni, mtsogoleri wa fuko la Yuda.
Y Ram engendró a Aminadab; y Aminadab engendró a Naasón, príncipe de los hijos de Judá;
11 Naasoni anabereka Salima, Salima anabereka Bowazi,
y Naasón engendró a Salmón, y Salmón engendró a Booz;
12 Bowazi anabereka Obedi ndipo Obedi anabereka Yese.
y Booz engendró a Obed, y Obed engendró a Isaí;
13 Yese anabereka Eliabu mwana wake woyamba, wachiwiri Abinadabu, wachitatu Simea,
e Isaí engendró a Eliab, su primogénito, y el segundo Abinadab, y Simea el tercero;
14 wachinayi Netaneli, wachisanu Radai,
el cuarto Natanael, el quinto Radai;
15 wachisanu ndi chimodzi Ozemu ndi wachisanu ndi chiwiri Davide.
el sexto Ozem, el séptimo David;
16 Alongo awo anali Zeruya ndi Abigayeli. Ana atatu a Zeruya anali Abisai Yowabu ndi Asaheli.
de los cuales Sarvia y Abigail fueron hermanas. Los hijos de Sarvia fueron tres: Abisai, Joab, y Asael.
17 Abigayeli anali amayi ake a Amasa amene abambo ake anali Yeteri wa fuko la Ismaeli.
Abigail engendró a Amasa, cuyo padre fue Jeter ismaelita.
18 Kalebe mwana wa Hezironi anabereka ana mwa Azuba mkazi wake (ndi mwa Yerioti). Ana a mkaziyo anali awa: Yeseri, Sobabu ndi Aridoni.
Caleb hijo de Hezrón engendró a Jeriot de su mujer Azuba. Y los hijos de ella fueron Jeser, Sobad, y Ardón.
19 Azuba atamwalira, Kalebe anakwatira Efurata, amene anamuberekera Huri.
Y muerta Azuba, tomó Caleb por mujer a Efrata, la cual le dio a luz a Hur.
20 Huri anabereka Uri ndipo Uri anabereka Bezaleli.
Y Hur engendró a Uri, y Uri engendró a Bezaleel.
21 Patapita nthawi, Hezironi anagona ndi mwana wamkazi wa Makiri abambo ake a Giliyadi (iye anamukwatira ali ndi zaka 60) ndipo anamuberekera Segubu.
Después entró Hezrón a la hija de Maquir padre de Galaad, la cual tomó siendo él de sesenta años, y ella le dio a luz a Segub.
22 Segubu anabereka Yairi, amene anali ndi mizinda 23 ku Giliyadi.
Y Segub engendró a Jair, el cual tuvo veintitrés ciudades en la tierra de Galaad.
23 (Koma Gesuri ndi Aramu analanda Havoti Yairi komanso Kenati ndi madera ake onse ozungulira, mizinda makumi asanu ndi umodzi). Onsewa anali adzukulu, a Makiri abambo ake a Giliyadi.
Y Gesur y Aram tomaron las ciudades de Jair de ellos, y a Kenat con sus aldeas, sesenta lugares. Todos estos fueron de los hijos de Maquir padre de Galaad.
24 Atamwalira Hezironi ku Kalebe Efurata, Abiya mkazi wa Hezironi anamuberekera Asihuri abambo a Tekowa.
Y muerto Hezrón en Caleb de Efrata ( Belén ), Abías mujer de Hezrón le dio a luz a Asur padre de Tecoa.
25 Ana a Yerahimeeli, mwana woyamba wa Hezironi anali: Ramu, mwana wake woyamba, Buna, Oreni, Ozemu ndi Ahiya.
Y los hijos de Jerameel primogénito de Hezrón fueron Ram su primogénito, Buna, Orén, Ozem, y Ahías.
26 Yerahimeeli anali ndi mkazi wina amene dzina lake linali Atara, amene anali amayi a Onamu.
Y tuvo Jerameel otra mujer llamada Atara, que fue madre de Onam.
27 Ana a Ramu, mwana woyamba wa Yerahimeeli, anali awa: Maazi, Yamini ndi Ekeri.
Y los hijos de Ram primogénito de Jerameel fueron Maaz, Jamín, y Equer.
28 Ana a Onamu anali awa: Shamai ndi Yada. Ana a Shamai anali awa: Nadabu ndi Abisuri.
Y los hijos de Onam fueron Samai, y Jada. Los hijos de Samai: Nadab, y Abisur.
29 Mkazi wa Abisuri anali Abihaili, amene anamuberekera Ahibani ndi Molidi.
Y el nombre de la mujer de Abisur fue Abihail, la cual le dio a luz a Ahbán, y a Molid.
30 Ana a Nadabu anali awa: Seledi ndi Apaimu. Koma Seledi anamwalira wopanda ana.
Y los hijos de Nadab: Seled y Apaim. Y Seled murió sin hijos.
31 Ana a Apaimu anali awa: Isi, amene anabereka Sesani. Sesani anabereka Ahilai.
E Isi fue hijo de Apaim; y Sesán, hijo de Isi; e hijo de Sesán, Ahlai.
32 Ana a Yada, mʼbale wa Samai, anali awa: Yereri ndi Yonatani. Koma Yeteri anamwalira wopanda ana.
Los hijos de Jada hermano de Samai: Jeter y Jonatán. Y murió Jeter sin hijos.
33 Ana a Yonatani anali awa: Peleti ndi Zaza. Amenewa anali adzukulu a Yerahimeeli.
Y los hijos de Jonatán: Pelet, y Zaza. Estos fueron los hijos de Jerameel.
34 Sesani sanabereke ana aamuna koma aakazi okhaokha. Iye anali ndi wantchito wa ku Igupto, dzina lake Yariha.
Y Sesán no tuvo hijos, sino hijas.
35 Sesani anapereka mwana wake wamkazi kwa Yariha wantchito wake kuti amukwatire ndipo anamuberekera Atayi.
Y tuvo Sesán un siervo Egipcio, llamado Jarha, al cual dio Sesán por mujer a su hija; y ella le dio a luz a Atai.
36 Atayi anali abambo ake a Natani, Natani anali abambo ake a Zabadi,
Y Atai engendró a Natán, y Natán engendró a Zabad;
37 Zabadi anali abambo a Efilali, Efilali anali abambo a Obedi,
y Zabad engendró a Eflal, y Eflal engendró a Obed;
38 Obedi anali abambo a Yehu, Yehu anali abambo a Azariya,
y Obed engendró a Jehú, y Jehú engendró a Azarías;
39 Azariya anali abambo a Helezi, Helezi anali abambo a Eleasa,
y Azarías engendró a Heles, Heles engendró a Elasa;
40 Eleasa anali abambo ake a Sisimai, Sisimai anali abambo a Salumu,
Elasa engendró a Sismai, y Sismai engendró a Salum;
41 Salumu anali abambo a Yekamiya, Yekamiya anali abambo a Elisama.
y Salum engendró a Jecamías, y Jecamías engendró a Elisama.
42 Ana a Kalebe mʼbale wa Yerahimeeli anali awa: Mesa mwana wachisamba, anali abambo a Zifi, ndipo mwana wake Maresa anali abambo a Hebroni.
Los hijos de Caleb hermano de Jerameel fueron: Mesa su primogénito, que fue el padre de Zif; y de sus otros hijos, Maresa, padre de Hebrón.
43 Ana a Hebroni anali awa: Kora, Tapuwa, Rekemu ndi Sema.
Y los hijos de Hebrón: Coré, y Tapúa, y Requem, y Sema.
44 Sema anali abambo ake Rahamu ndipo Rahamu anali abambo a Yorikeamu. Rekemu anali abambo a Samai.
Y Sema engendró a Raham, padre de Jorcoam; y Requem engendró a Samai.
45 Mwana wa Samai anali Maoni, ndipo Maoni anali abambo a Beti Zuri.
Maón fue hijo de Samai, y Maón padre de Bet-sur.
46 Efai, mzikazi wa Kalebe, anali amayi a Harani, Moza ndi Gazezi. Harani anali abambo a Gazezi.
Y Efa, concubina de Caleb, le dio a luz a Harán, y a Mosa, y a Gazez. Y Harán engendró a Gazez.
47 Ana a Yahidai anali awa: Regemu, Yotamu, Gesani, Peleti, Efai ndi Saafi.
Y los hijos de Jahdai: Regem, Jotam, Gesam, Pelet, Efa, y Saaf.
48 Maaka mzikazi wa Kalebe anali mayi Seberi ndi Tirihana.
Maaca, concubina de Caleb, le dio a luz a Seber, y a Tirhana.
49 Iye anaberekanso Saafi abambo a Madimena ndi Seva abambo a Makibena ndi Gibeya. Mwana wamkazi wa Kalebe anali Akisa.
Y también le dio a luz a Saaf padre de Madmana, y a Seva padre de Macbena, y padre de Gibea. Y Acsa fue hija de Caleb.
50 Izi zinali zidzukulu za Kalebe. Ana a Huri mwana wachisamba wa Efurata anali awa: Sobala abambo a Kiriati Yearimu,
Estos fueron los hijos de Caleb, hijo de Hur, primogénito de Efrata: Sobal, padre de Quiriat-jearim;
51 Salima abambo a Betelehemu ndi Harefu abambo ake a Beti-Gadera.
Salma, padre de Belén; Haref, padre de Bet-gader.
52 Zidzukulu za Sobala abambo a Kiriati Yearimu zinali izi: Harowe, theka la banja la Manahati,
Y los hijos de Sobal padre de Quiriat-jearim, el cual era señor de la mitad de Hamenuhot.
53 ndipo mabanja a Kiriati-Yeyarimu anali awa: Aitiri, Aputi, Asumati ndi Amisirai. Azorati ndi Aesitaoli anachokera kwa amenewa.
Y las familias de Quiriat-jearim fueron los itritas, y los futitas, y los sumatitas, y los misraítas; de los cuales salieron los zoratitas, y los estaolitas.
54 Zidzukulu za Salima zinali izi: Betelehemu, Anetofati, Atiroti-Beti-Yowabu, theka la banja la Manahati, Azori,
Los hijos de Salma: Belén, y los netofatitas, los cuales son las coronas de la casa de Joab, y de la mitad de los manahetitas, los zoraítas.
55 ndiponso mabanja a alembi amene amakhala ku Yabesi: Atiroti, Asimeati ndiponso Asukati. Awa ndi Akeni amene anachokera kwa Hamati, kholo la Arekabu.
Y las familias de los escribas, que moraban en Jabes, fueron los tirateos, simeateos, sucateos; los cuales son los ceneos que vinieron de Hamat, padre de la casa de Recab.

< 1 Mbiri 2 >