< 1 Mbiri 2 >

1 Ana a Israeli anali awa: Rubeni, Simeoni, Levi, Yuda, Isakara, Zebuloni,
Ovo su sinovi Izrailjevi: Ruvim, Simeun, Levije i Juda, Isahar i Zavulon,
2 Dani, Yosefe, Benjamini, Nafutali, Gadi ndi Aseri.
Dan, Josif i Venijamin, Neftalim, Gad i Asir.
3 Ana a Yuda anali awa: Eri, Onani ndi Sela. Ana atatu awa anabereka ndi mkazi wa Chikanaani, Batisuwa. Eri, mwana woyamba wa Yuda anali woyipa kwambiri pamaso pa Yehova, kotero Yehova anamupha.
Sinovi Judini: Ir i Avnan i Sila; ta mu tri rodi kæi Suvina Hananejka; ali Ir prvenac Judin bješe nevaljao pred Gospodom, te ga ubi.
4 Mpongozi wake Tamara anamuberekera Perezi ndi Zera. Ana onse a Yuda analipo asanu.
A Tamara snaha njegova rodi mu Faresa i Zaru. Svega pet bješe sinova Judinijeh.
5 Ana a Perezi anali awa: Hezironi ndi Hamuli.
Sinovi Faresovi: Esron i Amul.
6 Ana a Zera anali awa: Zimuri, Etani, Hemani, Kalikoli ndi Dara. Onse analipo asanu.
A sinovi Zarini: Zimrije i Etan i Eman i Halkol i Dara; svega pet.
7 Mwana wa Karimi anali Akani, amene anabweretsa mavuto pakati pa Israeli pamene anatenga zinthu zoyenera kuwonongedwa.
I sinovi Harmijini: Ahan, koji smuti Izrailja ogriješiv se o stvari proklete.
8 Mwana wa Etani anali Azariya.
A sinovi Etanovi: Azarija.
9 Ana amene anabadwa kwa Hezironi anali: Yerahimeeli, Ramu ndi Kelubai.
A sinovi Esronovi, što mu se rodiše: Jerameilo i Aram i Halev.
10 Ramu anabereka Aminadabu ndipo Aminadabu anali abambo ake a Naasoni, mtsogoleri wa fuko la Yuda.
A Aram rodi Aminadava, a Aminadav rodi Nasona, kneza sinova Judinijeh;
11 Naasoni anabereka Salima, Salima anabereka Bowazi,
A Nason rodi Salmona; a Salmon rodi Voza;
12 Bowazi anabereka Obedi ndipo Obedi anabereka Yese.
A Voz rodi Ovida; a Ovid rodi Jeseja;
13 Yese anabereka Eliabu mwana wake woyamba, wachiwiri Abinadabu, wachitatu Simea,
A Jesej rodi prvenca svojega Elijava, i Avinadava drugoga i Samu treæega,
14 wachinayi Netaneli, wachisanu Radai,
Natanaila èetvrtoga, Radaja petoga,
15 wachisanu ndi chimodzi Ozemu ndi wachisanu ndi chiwiri Davide.
Osema šestoga, Davida sedmoga,
16 Alongo awo anali Zeruya ndi Abigayeli. Ana atatu a Zeruya anali Abisai Yowabu ndi Asaheli.
I sestre im Seruju i Avigeju. A sinovi Serujini bjehu Avisaj i Joav i Asailo, trojica.
17 Abigayeli anali amayi ake a Amasa amene abambo ake anali Yeteri wa fuko la Ismaeli.
A Avigeja rodi Amasu; a otac Amasin bješe Jeter Ismailjac.
18 Kalebe mwana wa Hezironi anabereka ana mwa Azuba mkazi wake (ndi mwa Yerioti). Ana a mkaziyo anali awa: Yeseri, Sobabu ndi Aridoni.
A Halev sin Esronov rodi s Azuvom ženom svojom i s Jeriotom sinove, i sinovi mu bjehu Jeser i Sovav i Ardon.
19 Azuba atamwalira, Kalebe anakwatira Efurata, amene anamuberekera Huri.
A kad umrije Azuva, Halev se oženi Efratom, koja mu rodi Ora;
20 Huri anabereka Uri ndipo Uri anabereka Bezaleli.
A Or rodi Uriju, a Urija rodi Veseleila.
21 Patapita nthawi, Hezironi anagona ndi mwana wamkazi wa Makiri abambo ake a Giliyadi (iye anamukwatira ali ndi zaka 60) ndipo anamuberekera Segubu.
Potom otide Esron ka kæeri Mahira oca Galadova, i oženi se njom kad mu bijaše šezdeset godina, i ona mu rodi Seguva.
22 Segubu anabereka Yairi, amene anali ndi mizinda 23 ku Giliyadi.
A Seguv rodi Jaira, koji imaše dvadeset i tri grada u zemlji Galadskoj.
23 (Koma Gesuri ndi Aramu analanda Havoti Yairi komanso Kenati ndi madera ake onse ozungulira, mizinda makumi asanu ndi umodzi). Onsewa anali adzukulu, a Makiri abambo ake a Giliyadi.
Jer uze Gesurejima i Sircima sela Jairova i Kenat sa selima njegovijem, šezdeset gradova. To sve uzeše sinovi Mahira oca Galadova.
24 Atamwalira Hezironi ku Kalebe Efurata, Abiya mkazi wa Hezironi anamuberekera Asihuri abambo a Tekowa.
I kad umrije Esron u Halev-Efrati, žena Esronova Avija rodi mu Ashora oca Tekojanima.
25 Ana a Yerahimeeli, mwana woyamba wa Hezironi anali: Ramu, mwana wake woyamba, Buna, Oreni, Ozemu ndi Ahiya.
A sinovi Jerameila prvenca Esronova bjehu: prvenac Aram, pa Vuna i Oren i Osem i Ahija.
26 Yerahimeeli anali ndi mkazi wina amene dzina lake linali Atara, amene anali amayi a Onamu.
Imaše i drugu ženu Jerameilo, po imenu Ataru, ona je mati Onamova.
27 Ana a Ramu, mwana woyamba wa Yerahimeeli, anali awa: Maazi, Yamini ndi Ekeri.
A sinovi Arama prvenca Jerameilova bjehu: Mas i Jamin i Eker.
28 Ana a Onamu anali awa: Shamai ndi Yada. Ana a Shamai anali awa: Nadabu ndi Abisuri.
I sinovi Onamovi bjehu: Samaj i Jadaj; a sinovi Samajevi: Nadav i Avisur.
29 Mkazi wa Abisuri anali Abihaili, amene anamuberekera Ahibani ndi Molidi.
I ime ženi Avisurovoj bješe Avihaila, koja mu rodi Avana i Molida.
30 Ana a Nadabu anali awa: Seledi ndi Apaimu. Koma Seledi anamwalira wopanda ana.
A sinovi Nadavovi: Seled i Apaim; ali Seled umrije bez djece.
31 Ana a Apaimu anali awa: Isi, amene anabereka Sesani. Sesani anabereka Ahilai.
A sinovi Apailovi: Jesej; a sinovi Jesejevi: Sisan, i kæi Sisanova Alaja.
32 Ana a Yada, mʼbale wa Samai, anali awa: Yereri ndi Yonatani. Koma Yeteri anamwalira wopanda ana.
A sinovi Jadaja brata Samajeva: Jeter i Jonatan; ali Jeter umrije bez djece.
33 Ana a Yonatani anali awa: Peleti ndi Zaza. Amenewa anali adzukulu a Yerahimeeli.
A sinovi Jonatanovi: Falet i Zaza. Ti bijahu sinovi Jerameilovi.
34 Sesani sanabereke ana aamuna koma aakazi okhaokha. Iye anali ndi wantchito wa ku Igupto, dzina lake Yariha.
A Sisan ne imaše sinova nego kæeri; i imaše Sisan slugu Misirca po imenu Jaraju.
35 Sesani anapereka mwana wake wamkazi kwa Yariha wantchito wake kuti amukwatire ndipo anamuberekera Atayi.
Zato Sisan dade kæer svoju Jaraji sluzi svojemu za ženu; a ona mu rodi Ataja.
36 Atayi anali abambo ake a Natani, Natani anali abambo ake a Zabadi,
A Ataj rodi Natana; a Natan rodi Zavada;
37 Zabadi anali abambo a Efilali, Efilali anali abambo a Obedi,
A Zavad rodi Eflala; a Eflal rodi Ovida;
38 Obedi anali abambo a Yehu, Yehu anali abambo a Azariya,
A Ovid rodi Juja; a Juj rodi Azariju;
39 Azariya anali abambo a Helezi, Helezi anali abambo a Eleasa,
A Azarija rodi Helisa; a Helis rodi Eleasu;
40 Eleasa anali abambo ake a Sisimai, Sisimai anali abambo a Salumu,
A Eleasa rodi Sisamaja; a Sisamaj rodi Saluma;
41 Salumu anali abambo a Yekamiya, Yekamiya anali abambo a Elisama.
A Salum rodi Jekamiju; a Jekamija rodi Elisama.
42 Ana a Kalebe mʼbale wa Yerahimeeli anali awa: Mesa mwana wachisamba, anali abambo a Zifi, ndipo mwana wake Maresa anali abambo a Hebroni.
A sinovi Haleva brata Jerameilova bjehu: Misa prvenac njegov, otac Zifejima; pa sinovi Marise oca Hevronova.
43 Ana a Hebroni anali awa: Kora, Tapuwa, Rekemu ndi Sema.
A sinovi Hevronovi: Korej i Tafuja i Rekem i Sema.
44 Sema anali abambo ake Rahamu ndipo Rahamu anali abambo a Yorikeamu. Rekemu anali abambo a Samai.
A Sema rodi Rama oca Jorkoamova; a Rekem rodi Samaja.
45 Mwana wa Samai anali Maoni, ndipo Maoni anali abambo a Beti Zuri.
A sin Samajev bješe Maon, a taj Maon bi otac Vet-Suru.
46 Efai, mzikazi wa Kalebe, anali amayi a Harani, Moza ndi Gazezi. Harani anali abambo a Gazezi.
I Gefa inoèa Halevova rodi Harana i Mosu i Gazesa.
47 Ana a Yahidai anali awa: Regemu, Yotamu, Gesani, Peleti, Efai ndi Saafi.
A sinovi Jadajevi: Regem i Jotam i Gisan i Felet i Gefa i Sagaf.
48 Maaka mzikazi wa Kalebe anali mayi Seberi ndi Tirihana.
Maha inoèa Halevova rodi Severa i Tirhanu.
49 Iye anaberekanso Saafi abambo a Madimena ndi Seva abambo a Makibena ndi Gibeya. Mwana wamkazi wa Kalebe anali Akisa.
Rodi i Sagafa oca Madmancima i Sevu oca Mahvincima i Gavajanima; a kæi Halevova bijaše Ahsa.
50 Izi zinali zidzukulu za Kalebe. Ana a Huri mwana wachisamba wa Efurata anali awa: Sobala abambo a Kiriati Yearimu,
Ovo bijahu sinovi Haleva sina Ora prvenca Efratina; Soval otac Kirijat-Jarimu,
51 Salima abambo a Betelehemu ndi Harefu abambo ake a Beti-Gadera.
Salma otac Vitlejemu, Aref otac Vet-Gaderu.
52 Zidzukulu za Sobala abambo a Kiriati Yearimu zinali izi: Harowe, theka la banja la Manahati,
A imaše sinove Soval otac Kirijat-Jarimu: Aroja i Asi-Amenuhota.
53 ndipo mabanja a Kiriati-Yeyarimu anali awa: Aitiri, Aputi, Asumati ndi Amisirai. Azorati ndi Aesitaoli anachokera kwa amenewa.
A porodice Kirijat-jarimske bjehu: Jetrani i Fuæani i Sumaæani i Misrajani. Od njih izidoše Saraæani i Estaoljani.
54 Zidzukulu za Salima zinali izi: Betelehemu, Anetofati, Atiroti-Beti-Yowabu, theka la banja la Manahati, Azori,
Sinovi Salmini: Vitlejemci i Netofaæani, Ataroæani od doma Joavova, i Zorani, polovina Manahaæana,
55 ndiponso mabanja a alembi amene amakhala ku Yabesi: Atiroti, Asimeati ndiponso Asukati. Awa ndi Akeni amene anachokera kwa Hamati, kholo la Arekabu.
I porodice pisarske u Javisu, Tiraæani, Simeaæani, Suhaæani; to su Keneji, koji se narodiše od Emata, oca doma Rihavova.

< 1 Mbiri 2 >