< 1 Mbiri 1 >

1 Adamu, Seti, Enosi
Adam, Seth, Enos,
2 Kenani, Mahalaleli, Yaredi,
Caïnan, Malalehel, Jared,
3 Enoki, Metusela, Lameki, Nowa.
Enoch, Mathusalem, Larnech, Noé.
4 Ana a Nowa, Semu, Hamu ndi Yafeti.
Fils de Noé: Sem, Cham, Japheth.
5 Ana aamuna a Yafeti anali: Gomeri, Magogi, Madai, Yavani, Tubala, Mesaki ndi Tirasi.
Fils de Japheth: Corner, Magog, Madaï, Javan, Elisa, Thobel, Mosoch et Thiras.
6 Ana aamuna a Gomeri anali: Asikenazi, Rifati ndi Togarima
Fils de Gomer: Ascenez, Rhiphath et Thorgama.
7 Ana aamuna a Yavani anali: Elisa, Tarisisi, Kitimu ndi Rodanimu.
Fils de Javan: Elisa, Tharsis, les Citians et les Rhodiens.
8 Ana aamuna a Hamu anali: Kusi, Miziraimu, Puti ndi Kanaani
Fils de Cham: Chus, Mesraïm, Phuth et Chanaan.
9 Ana aamuna a Kusi anali: Seba, Havila, Sabita, Raama ndi Sabiteka Ana aamuna a Raama anali: Seba ndi Dedani.
Fils de Chus: Saba, Evila, Sabatha, Regma et Sabalhaca. Fils de Regma: Saba et Dadan.
10 Kusi anali abambo a Nimurodi amene anali wankhondo wamphamvu kwambiri pa dziko lapansi.
Et Chus engendra Nemrod; celui-ci commença à être puissant et chasseur sur la terre.
11 Igupto ndiye kholo la Aludi, Aanami, Alehabu, Anafutu,
Fils de Sem: Elam, Assur, Arphaxad,
12 Apaturusi, Akasilu (kumene kunachokera Afilisti) ndi Akafitori.
Fils de Sem: Elam, Assur, Arphaxad,
13 Kanaani anabereka mwana wake wachisamba Sidoni, ndipo anaberekanso Ahiti,
Fils de Sem: Elam, Assur, Arphaxad,
14 Ayebusi, Aamori, Agirigasi
Fils de Sem: Elam, Assur, Arphaxad,
15 Ahivi, Aariki, Asini
Fils de Sem: Elam, Assur, Arphaxad,
16 Aaravadi, Azemari ndi Ahamati.
Fils de Sem: Elam, Assur, Arphaxad,
17 Ana aamuna a Semu anali: Elamu, Asuri, Aripakisadi, Ludi ndi Aramu. Ana aamuna a Aramu anali: Uzi, Huri, Geteri ndi Mesaki.
Fils de Sem: Elam, Assur, Arphaxad,
18 Aripakisadi anabereka Sela ndipo Selayo anabereka Eberi:
Salé,
19 Eberi anabereka ana aamuna awiri: wina anamutcha Pelegi, chifukwa pa nthawiyo anthu a pa dziko lapansi anagawikana. Dzina la mʼbale wake linali Yokitani.
Salé,
20 Yokitani anabereka Alimodadi, Selefi, Hazari-Maveti, Yera,
Salé,
21 Hadoramu, Uzali, Dikila
Salé,
22 Obali, Abimaeli, Seba,
Salé,
23 Ofiri, Havila ndi Yobabu. Onsewa anali ana aamuna a Yokitani.
Salé,
24 Semu, Aripakisadi, Sela
Salé,
25 Eberi, Pelegi, Reu
Héber, Phaleg, Réhu,
26 Serugi, Nahori, Tera
Sarug, Nachor, Tharé.
27 ndi Abramu (amene ndi Abrahamu).
Abraham.
28 Ana a Abrahamu ndi awa: Isake ndi Ismaeli.
Fils d'Abraham: Isaac et Ismaël.
29 Zidzukulu zake zinali izi: Nebayoti ndiye anali mwana woyamba wa Ismaeli, kenaka Kedara, Adibeeli, Mibisamu,
Voici leurs familles: premier-né d'Ismaël: Nabaïoth, Cédar, Abdéel, Massan,
30 Misima, Duma, Masa, Hadadi, Tema,
Masma, Duala, Massi, Choddan, Thèman,
31 Yeturi, Nafisi ndi Kedema. Awa anali ana a Ismaeli.
Jethur, Naphis, Cedma; voilà les fils d'Ismaël.
32 Ana a Ketura mzikazi wa Abrahamu anali awa: Zimurani, Yokisani, Medani, Midiyani, Isibaki ndi Suwa. Ana a Yokisani ndi awa: Seba ndi Dedani
Fils de Cettura, concubine d'Abraham: elle lui enfanta: Zameran, Jezan, Madian, Madal, Jesboc et Sué. Fils de Jezan: Dedan et Saba.
33 Ana aamuna a Midiyani anali, Efai, Eferi, Hanoki, Abida ndi Elida. Onsewa anali zidzukulu za Ketura.
Fils de Madian: Gephar, Aphir, Enoch, Abida et Elduga; voilà tous les fils de Cettura.
34 Abrahamu anabereka Isake. Ana a Isake anali awa: Esau ndi Israeli.
Abraham engendra Isaac. Fils d'Isaac: Jacob et Esaü.
35 Ana aamuna a Esau anali awa: Elifazi, Reueli, Yeusi, Yolamu ndi Kora.
Fils d'Esaü: Eliphaz, Raguel, Jehul, Jeglon et Coré.
36 Ana a Elifazi anali awa: Temani, Omari, Zefo, Gatamu ndi Kenazi: Amene anabereka ndi Timna: Amaleki.
Fils d'Eliphaz: Thêman, Omar, Sophar, Gatham, Canez, Thamna et Amalec.
37 Ana a Reueli anali awa: Nahati, Zera, Sama ndi Miza.
Fils de Raguel: Nachoth, Zaré, Somé et Mozé.
38 Ana a Seiri anali awa: Lotani, Sobala, Zibeoni, Ana, Disoni, Ezeri ndi Disani.
Fils de Seïr: Lotan, Sobal, Sébégon, Ana, Dison, Asar et Rison.
39 Ana aamuna a Lotani anali awa: Hori ndi Homamu. Timna anali mlongo wake wa Lotani.
Fils de Lotan: Horri et Héman; sœur de Lotan, Thamna.
40 Ana aamuna a Sobala anali awa: Alivani, Manahati, Ebala, Sefo ndi Onamu. Ana aamuna a Zibeoni anali awa: Ayiwa ndi Ana.
Fils de Sobal: Alon, Machanath, Tébel, Sophi et Onan. Fils de Sébégon: Eth et Sonan.
41 Mwana wa Ana anali Disoni. Ana a Disoni anali awa: Hemudani, Esibani, Itirani ndi Kerani
Fils de Sonan: Dison. Fils de Dison: Emeron, Asebon, Jethram et Harran.
42 Ana aamuna a Ezeri anali awa: Bilihani, Zaavani ndi Yaakani. Ana aamuna a Disani anali awa: Uzi ndi Arani.
Fils d'Asar: Balaam, Zucam, Acan. Fils de Bison, Os et Aran.
43 Awa ndi mafumu amene ankalamulira dziko la Edomu, mfumu iliyonse ya Israeli isanayambe kulamulira kumeneko: Bela mwana wa Beori, mzinda wake ankawutcha Dinihaba.
Et voici leurs rois: Balac, fils de Béor; le nom de sa ville est Dennaba.
44 Bela atamwalira, Yobabu mwana wa Zera wochokera ku Bozira analowa ufumu mʼmalo mwake.
Balac mourut, et Jobab, fils de Zara de Bosora, régna à sa place.
45 Yobabu atamwalira, Husamu wochokera ku dziko la Atemani, analowa ufumu mʼmalo mwake.
Jobab mourut, et Asom, de la terre des Thêmanites, régna à sa place.
46 Husamu atamwalira, Hadadi mwana wa Bedadi, amene anagonjetsa Amidiyani mʼdziko la Mowabu, analowa ufumu mʼmalo mwake. Mzinda wake unkatchedwa Aviti.
Asom mourut, et Adad, fils de Barad, régna à sa place; ce fut lui qui vainquit Madian dans le champ de Moab; le nom de sa ville est Gethaim.
47 Hadadi atamwalira, Samila wochokera ku Masireka analowa ufumu mʼmalo mwake.
Adad mourut, et Sebla (Samada) de Maseca régna à sa place.
48 Samila atamwalira, Sauli wochokera ku Rehoboti wa ku Mtsinje analowa ufumu mʼmalo mwake.
Sebla mourut, et Saul de Rooboth, sur l'Euphrate, régna à sa place.
49 Sauli atamwalira, Baala-Hanani mwana wa Akibori analowa ufumu mʼmalo mwake.
Saul mourut, et Balaennor (Ballanan), fils d'Achobor, régna à sa place.
50 Pamene Baala-Hanani anamwalira, Hadadi analowa ufumu mʼmalo mwake. Mzinda wake unkatchedwa Pau, ndipo dzina la mkazi wake linali Mehatabeli mwana wa Matiredi, mwana wamkazi wa Me-Zahabu.
Balaennor mourut, et Arad, fils de Barad, régna à sa place; le nom de sa ville est Phogor.
51 Hadadi anamwaliranso. Mafumu a ku Edomu anali: Timna, Aliva, Yeteti,
Chefs d'Edom: le chef Thaman (Thamna), le chef Golada (Gola), le chef Jéther,
52 Oholibama, Ela, Pinoni,
Le chef Elibamas (Olibema), le chef Ela, le chef Phinon,
53 Kenazi, Temani, Mibezari,
Le chef Cenez, le chef Théman, le chef Bassor (Mazar),
54 Magidieli ndi Iramu. Awa anali mafumu a ku Edomu.
Le chef Magediel, le chef Zaphoin: voilà les chefs d'Edom.

< 1 Mbiri 1 >