< ᏉᎳ ᏕᏏᎶᏂᎦ ᎠᏁᎯ ᏔᎵᏁ ᏧᏬᏪᎳᏁᎸᎯ 3 >

1 ᎤᎵᏍᏆᎸᏗᏃ ᎨᏒᎢ, ᎢᏓᎵᏅᏟ, ᎢᏣᏓᏙᎵᏍᏗᏍᎨᏍᏗ ᎠᏴ ᏍᎩᏯᏅᏓᏗᏍᎨᏍᏗ, ᎾᏍᎩ ᎧᏃᎮᏛ ᎤᎬᏫᏳᎯ ᎤᏤᎵᎦ ᎤᏰᎵᎯᏍᏗᏱ, ᎠᎴ ᎦᎸᏉᏗᏳ ᎢᏳᎵᏍᏙᏗᏱ, ᎾᏍᎩᏯ ᏥᏄᏍᏗ ᏂᎯ ᎢᏤᎲᎢ;
Potsiriza, abale, mutipempherere kuti uthenga wa Ambuye ufalikire msanga ndi kulemekezedwa monga momwe munachitira inu.
2 ᎠᎴ ᎾᏍᎩ ᏦᏣᏚᏓᎳᎡᏗᏱ ᎤᏂᏲ ᎠᎴ ᎠᏂᏍᎦᎾ ᎠᏂᏍᎦᏯ; ᎥᏝᏰᏃ ᎾᏂᎥ ᎪᎯᏳᏗ ᎨᏒ ᏳᏁᎭ.
Ndipo pempherani kuti tilanditsidwe mʼmanja mwa anthu ovuta ndi oyipa, pakuti si onse amene ali nacho chikhulupiriro.
3 ᎤᎬᏫᏳᎯᏍᎩᏂ ᏄᏓᎵᏓᏍᏛᎾ, ᎾᏍᎩ ᏨᏓᏣᎵᏂᎪᎯᏍᏔᏂ, ᎠᎴ ᏨᎵᏥᏲᏍᏙᏓᏁᎵ ᎤᏲ ᎢᏣᏛᏁᏗᏱ.
Koma Ambuye ndi wokhulupirika, ndipo adzakulimbikitsani ndi kukutetezani kwa woyipayo.
4 ᎠᎴ ᎣᏣᎵᏍᎦᏍᏙᏗ ᎤᎬᏫᏳᎯ ᏂᎯ ᎨᏒ ᎤᎬᏩᎵ, ᎾᏍᎩ ᏂᏣᏛᏁᎲᎢ, ᎠᎴ ᎠᏎ ᎾᏍᎩ ᎢᏣᏛᏁᏗ ᎨᏒ ᏄᏍᏛ ᎢᏨᏁᏤᎲᎢ.
Tili ndi chikhulupiriro mwa Ambuye kuti mukuchita zonse ndipo mudzapitirira kuchita zimene tinakulamulirani.
5 ᎠᎴ ᎤᎬᏫᏳᎯ ᏧᏎᎮᏗ ᎨᏎᏍᏗ ᏗᏥᎾᏫ ᎡᏥᎨᏳᎢ ᎢᏳᎵᏍᏙᏗᏱ ᎤᏁᎳᏅᎯ, ᎠᎴ ᏗᏨᏂᏗᏳ ᎢᏳᎵᏍᏙᏗᏱ ᎦᎶᏁᏛ ᎾᏍᎩᏯᎢ.
Ambuye atsogolere mitima yanu kuti mudziwe chikondi cha Mulungu ndiponso kupirira kumene Khristu amapereka.
6 ᎿᎭᏉᏃ ᎢᏨᏁᏤᎭ, ᎢᏓᎵᏅᏟ, ᎣᏨᏗᎭ ᏚᏙᎥ ᎢᎦᏤᎵ ᎤᎬᏫᏳᎯ ᏥᏌ ᎦᎶᏁᏛ, ᎾᏍᎩ ᏗᏣᏓᏓᎴᏓᏁᏗᏱ ᎾᏂᎥ ᎠᎾᎵᏅᏟ ᎤᏣᏘᏂ ᎢᏯᎾᏛᏁᎵᏙᎯ, ᎠᎴ ᏂᏓᏂᎧᎿᎭᏩᏕᎬᎾ ᏗᏕᏲᏗ ᎨᏒ ᎠᏴ ᏗᎪᎦᏓᏂᎸᏤᎸᎯ,
Abale, tikukulamulani mʼdzina la Ambuye Yesu Khristu, kuti mupewe mʼbale aliyense amene ndi waulesi ndi wachisokonezo, wosafuna kutsata zimene tinakuphunzitsani.
7 ᎢᏳᏒᏰᏃ ᎢᏥᎦᏔᎭ ᎢᏣᏛᏁᏗᏱ ᏍᎩᏍᏓᏩᏛᏍᏗᏱ; ᎥᏝᏰᏃ ᎤᏣᏘᏂ ᏱᏃᏣᏛᏁᎵᏙᎮ ᎢᏨᏰᎳᏗᏙᎲᎢ;
Pakuti inu mukudziwa zimene muyenera kuchita pofuna kutitsatira. Ife sitinali alesi pamene tinali nanu
8 ᎥᏝ ᎠᎴ ᎩᎶ ᎠᏎᏉ ᏲᏣᎵᏍᏓᏴᎾᏁᎮᎢ; ᏙᎩᎸᏫᏍᏓᏁᎲᎩᏍᎩᏂ ᎠᎴ ᏙᎩᏯᏪᏥᏙᎲᎩ ᎬᏩᎩᏨᏗ, ᏃᎦᏚᎵᏍᎬᎾ ᎨᏒ ᎢᏳᏍᏗ ᎠᏴ ᎠᏏᏴᏫ ᏂᏣᏛᏅ ᎦᎨᏛ ᎢᏲᏨᏴᏁᏗᏱ;
ndipo sitinadye chakudya cha aliyense osalipira. Komatu tinkagwira ntchito mwamphamvu usiku ndi usana kuti tisakhale cholemetsa kwa aliyense.
9 ᎥᏝ ᏃᎩᎲᎾ ᎨᏒ [ ᏅᏩᏓᎴ ᎢᏲᎦᏛᏁᏗᏱ ] ᏱᏅᏗᎦᎵᏍᏙᏗᏍᎨᎢ, ᏗᏣᏟᎶᏍᏙᏗᏍᎩᏂ ᏃᏣᏓᏛᏁᎲ ᎠᏴ ᏍᎩᏍᏓᏩᏛᏍᏗᏱ ᏅᏓᎦᎵᏍᏙᏗᏍᎬᎩ.
Sitinachite zimenezi chifukwa choti tinalibe mphamvu zolamula kuti mutithandize koma kuti tikhale chitsanzo choti mutsatire.
10 ᎾᎯᏳᏰᏃ ᏥᏨᏰᎳᏗᏙᎲᎩ, ᎯᎠ ᎾᏍᎩ ᏄᏍᏛᎩ ᎢᏨᏁᏤᎸᎩ, ᎾᏍᎩ ᎢᏳᏃ ᎩᎶ ᏄᏚᎵᏍᎬᎾ ᏱᎩ, ᏧᎸᏫᏍᏓᏁᏗᏱ ᎾᏍᏉ ᎤᎵᏍᏓᏴᏗᏱ ᏂᎨᏒᎾ ᎨᏒᎢ.
Pakuti ngakhale pamene tinali nanu, tinakupatsani lamulo lakuti, “Munthu wosafuna kugwira ntchito, asadye.”
11 ᎣᏣᏛᎩᎭᏰᏃ ᎾᏍᎩ ᎩᎶ ᎨᏣᏓᏑᏴ ᎤᏣᏘᏂ ᎾᎾᏛᏁᎵᏙᎲᎢ, ᎪᎱᏍᏗ ᎾᎾᏛᏁᎲᎾ, ᎠᏎᏃ ᎠᎾᏛᏁᎵᏙᎯ ᎢᎩ.
Ife tikumva kuti pakati panu pali ena amene ndi alesi. Iwo safuna kugwira ntchito, koma amangolowerera pa za eni.
12 ᎾᏍᎩᏃ ᎢᏳᎾᏍᏗ ᎨᏒᎢ, ᏙᏥᏁᏤᎭ ᎠᎴ ᏙᏥᏍᏗᏰᏗᎭ ᏙᏥᏁᎢᏍᏓᏁᎭ ᎢᎦᏤᎵ ᎤᎬᏫᏳᎯ ᏥᏌ ᎦᎶᏁᏛ, ᎾᏍᎩ ᏙᎯᏉ ᏧᏂᎸᏫᏍᏓᏁᏗᏱ, ᎠᎴ ᎤᏅᏒ ᎤᎾᏤᎵ ᎠᎵᏍᏓᏴᏗ ᎤᎾᎵᏍᏓᏴᏙᏗᏱ.
Mʼdzina la Ambuye Yesu Khristu, tikuwalamula ndi kuwakakamiza kuti azigwira ntchito mwabata ndi kumadya chakudya chodzigwirira ntchito okha.
13 ᏂᎯᏍᎩᏂ, ᎢᏓᎵᏅᏟ, ᏞᏍᏗ ᏱᏗᏥᏯᏪᎨᏍᏗ ᎣᏍᏛ ᏕᏥᎸᏫᏍᏓᏁᎲᎢ.
Koma inu abale, musatope nʼkuchita zabwino.
14 ᎢᏳᏃ ᎩᎶ ᏂᎪᎯᏳᎲᏍᎬᎾ ᎢᎨᏎᏍᏗ ᎣᏥᏬᏂᏍᎬ ᎠᏂ ᎣᏦᏪᎵᏍᎬᎢ, ᎬᏂᎨᏒ ᏁᏨᏁᎸᎭ ᎾᏍᎩ, ᎠᎴ ᏞᏍᏗ ᎢᏧᎳᎭ ᎢᏤᏙᎸᎩ, ᎾᏍᎩ ᎬᏩᏕᎰᎯᏍᏗ ᎢᏳᎵᏍᏙᏗᏱ.
Ngati wina aliyense akana kumvera malangizo athu a mʼkalatayi, mumuonetsetse ameneyo ndipo musayanjane naye kuti achite manyazi.
15 ᎠᏗᎾ ᏞᏍᏗ ᎡᏥᏍᎦᎩ ᎢᏳᏍᏗ ᏰᏣᏓᏅᏖᏍᎨᏍᏗ, ᎡᏥᎬᏍᎪᎸᎥᏍᎨᏍᏗᏍᎩᏂ ᎢᏣᏓᏅᏟ ᎾᏍᎩᏯᎢ.
Komatu musamutenge kukhala mdani, koma muchenjezeni ngati mʼbale.
16 ᎤᎬᏫᏳᎯᏃ ᏅᏩᏙᎯᏯᏛ ᎤᏪᎯ ᎤᏩᏒ ᎠᏎ ᎢᏥᏁᏗ ᎨᏎᏍᏗ ᏅᏩᏙᎯᏯᏛ ᏂᎪᎯᎸᎢ. ᎤᎬᏫᏳᎯ ᏂᏥᎥ ᏕᏥᎧᎿᎭᏗᏙᎮᏍᏗ.
Tsopano Ambuye mwini mtendere akupatseni mtendere nthawi zonse mwa njira iliyonse. Ambuye akhale ndi inu nonse.
17 ᎠᏴ ᏉᎳ ᎠᏆᏓᏲᎵᏍᏗ ᎨᏒ ᎠᏋᏒ ᎠᏉᏰᏂ ᎠᏋᏔᏅᎯ ᎠᏉᏪᎳᏅᎯ, ᎾᏍᎩ ᏗᎪᎵᏍᏙᏗ ᏥᎩ ᏂᎦᏛ ᎪᏪᎵ; ᎾᏍᎩᏯ ᏂᎬᏁᎰ ᎪᏪᎵᏍᎪᎢ.
Ine Paulo, ndikulemba malonje awa ndi dzanja langa, chimene ndi chizindikiro chodziwika mʼmakalata anga onse. Umo ndi mmene ndimalembera.
18 ᎬᏩᎦᏘᏯ ᎤᏓᏙᎵᏍᏗ ᎨᏒ ᎢᎦᏤᎵ ᎤᎬᏫᏳᎯ ᏥᏌ ᎦᎶᏁᏛ ᏕᏥᎧᎿᎭᏩᏗᏙᎮᏍᏗ ᏂᏥᎥᎢ. ᎡᎺᏅ.
Chisomo cha Ambuye athu Yesu Khristu chikhale ndi inu nonse.

< ᏉᎳ ᏕᏏᎶᏂᎦ ᎠᏁᎯ ᏔᎵᏁ ᏧᏬᏪᎳᏁᎸᎯ 3 >