< ᏣᏂ ᎢᎬᏱᏱ ᎤᏬᏪᎳᏅᎯ 5 >

1 ᎩᎶ ᏱᎪᎯᏳᎲᏍᎦ ᏥᏌ ᎾᏍᎩ ᎦᎶᏁᏛ ᎨᏒᎢ, ᎾᏍᎩ ᎤᏁᎳᏅᎯ ᎤᏕᏔᏅᎯ, ᎩᎶᏃ ᏳᎨᏳᎭ ᎤᏓᎾᏄᎪᏫᏒᎯ, ᎾᏍᏉ ᎠᏥᎾᏄᎪᏫᏒᎯ ᎤᎨᏳᎯᏳ ᎨᏐᎢ.
Aliyense amene amakhulupirira kuti Yesu ndi Khristu, iyeyo ndi mwana wa Mulungu, ndipo aliyense amene amakonda Atate amakondanso Mwana wake.
2 ᎤᏁᎳᏅᎯ ᎡᏗᎨᏳᎢ ᏥᎨᏐᎢ, ᎠᎴ ᏥᎩᏍᏆᏂᎪᏙ ᎤᏤᎵᎦ ᏗᎧᎿᎭᏩᏛᏍᏗ, ᎾᏍᎩ ᎢᏓᏙᎴᎰᎯᏍᏗᏍᎪ ᎨᏗᎨᏳᎢᏳ ᎨᏒ ᎤᏁᎳᏅᎯ ᏧᏪᏥ.
Chodziwira kuti timakonda ana a Mulungu nʼchakuti timakonda Mulungu ndi kusunga malamulo ake.
3 ᎾᏍᎩᏰᏃ ᎯᎠ ᏄᏍᏗ ᎤᏁᎳᏅᎯ ᎠᎨᏳᏗ ᎨᏒᎢ, ᎾᏍᎩ ᏗᎩᏍᏆᏂᎪᏙᏗᏱ ᏧᏤᎵ ᏗᎧᎿᎭᏩᏛᏍᏗ; ᎤᏤᎵᏃ ᏗᎧᎿᎭᏩᏛᏍᏗ ᎥᏝ ᎦᎨᏗᏳ ᏱᎩ.
Pakuti kukonda Mulungu ndiye kusunga malamulo ake. Ndipo malamulo ake siwolemetsa,
4 ᏂᎦᎥᏰᏃ ᎪᎱᏍᏗ ᎤᏁᎳᏅᎯ ᎤᏕᏔᏅᎯ ᎠᏎᎪᎩᏍᎪ ᎡᎶᎯ. ᎢᎪᎯᏳᏒᏃ ᎾᏍᎩ ᎠᏎᎪᎩᏍᎩ ᎡᎶᎯ.
chifukwa aliyense amene ndi mwana wa Mulungu amagonjetsa dziko lapansi. Chikhulupiriro chathu ndicho timagonjetsera dziko lapansi.
5 ᎦᎪ Ꮎ ᎡᎶᎯ ᎠᏎᎪᎩᏍᎩ ᎢᏳᏃ ᎾᏍᎩ ᏂᎨᏒᎾ ᏱᎩ ᎾᏍᎩ Ꮎ ᎪᎯᏳᎲᏍᎩ ᏥᏌ ᎤᏁᎳᏅᎯ ᎤᏪᏥ ᎨᏒᎢ?
Ndani amagonjetsa dziko lapansi? Yekhayo amene amakhulupirira kuti Yesu ndi Mwana wa Mulungu.
6 ᎾᏍᎩ ᎠᎹ ᎠᎴ ᎩᎬ ᎤᎷᎯᏍᏔᏅᎯ, ᎯᎠ ᏥᏌ ᎦᎶᏁᏛ; ᎥᏝ ᎠᎹᏉ ᎤᏩᏒ, ᎠᎹᏍᎩᏂ ᎠᎴ ᎩᎬ. ᎬᏩᏠᏯᏍᏗ ᎠᎴ ᎠᏓᏅᏙ ᎾᏍᎩ ᎧᏃᎮᏍᎩ, ᎠᏓᏅᏙᏰᏃ ᎦᏱᎪᎩ ᏂᎨᏒᎾ.
Uyu ndiye anabwera mwa madzi ndi magazi, ndiye Yesu Khristu. Sanabwere mwa madzi okha, koma mwa madzi ndi magazi. Ndipo ndi Mzimu Woyera amene akuchitira umboni, chifukwa Mzimu Woyera ndi choonadi.
7 ᎠᏂᏦᎢᏰᏃ ᎠᏂᏃᎮᏍᎩ ᎦᎸᎳᏗ; ᎠᎦᏴᎵᎨᎢ, ᎧᏃᎮᏛ, ᎦᎸᏉᏗᏳᏃ ᎠᏓᏅᏙ; ᎾᏍᎩᏃ ᎯᎠ ᎠᏂᏦᎢ ᎨᏒ ᏌᏉᏉ.
Pakuti pali atatu amene amachitira umboni.
8 ᎠᏂᏦᎢᏃ ᎠᏂᏃᎮᏍᎩ ᎡᎶᎯ, ᎠᏓᏅᏙ, ᎠᎹ, ᎠᎴ ᎩᎬ, ᎾᏍᎩᏃ ᎯᎠ ᎠᏂᏦᎢ ᎨᏒ ᎤᏠᏱ ᎠᏂᏃᎮᎭ.
Mzimu Woyera, madzi ndi magazi; ndipo atatu amavomerezana.
9 ᎢᏳᏃ ᏱᏗᏗᏂᏱᎭ ᏴᏫ ᎤᏂᏃᎮᎸᎯ, ᎤᏁᎳᏅᎯ ᎤᏃᎮᎸᎯ ᎤᏟ ᎦᎸᏉᏗᏳ; ᎯᎠᏰᏃ ᎾᏍᎩ ᎤᏁᎳᏅᎯ ᎤᏃᎮᎸᎯ, ᎾᏍᎩ ᎤᏁᎢᏍᏔᏅᎯ ᏥᎩ ᎤᏪᏥ.
Timalandira umboni wa anthu, koma umboni wa Mulungu ndi wopambana. Umboniwo ndi umene anachitira Mwana wake.
10 ᎪᎯᏳᎲᏍᎩ ᎤᏁᎳᏅᎯ ᎤᏪᏥ ᎾᏍᎩ ᎤᏩᏒ ᎨᏒ ᎤᏪᎭ ᎪᎯᏳᏗᏍᎩ; ᎤᏁᎳᏅᎯ ᎪᎯᏳᎲᏍᎩ ᏂᎨᏒᎾ, ᎾᏍᎩ ᎤᏁᎳᏅᎯ ᎤᏰᎪᏅ, ᏅᏗᎦᎵ ᏍᏙᏗᎭ ᏂᎪᎯᏳᎲᏍᎬᎾ ᎨᏒ ᎤᏁᎳᏅᎯ ᎤᏃᎮᎸᎢ ᎤᏪᏥ ᎤᏁᎢᏍᏔᏅᎢ.
Aliyense amene amakhulupirira Mwana wa Mulungu ali nawo umboniwu mu mtima mwake, koma aliyense amene sanakhulupirire Mulungu amayesa kuti Mulunguyo ndi wonama, chifukwa sanakhulupirire umboni umene Mulungu anachitira wa Mwana wake.
11 ᎯᎠᏃ ᎾᏍᎩ ᏄᏍᏗ ᎧᏃᎮᎸᎯ ᎨᏒᎢ, ᎾᏍᎩ ᎤᏁᎳᏅᎯ ᎢᎩᏁᎸ ᏫᎾᏍᏛᎾ ᎬᏂᏛ, ᎠᎴ ᎾᏍᎩ ᎯᎠ ᎬᏂᏛ ᎤᏪᏥ ᎤᏤᎵᎦ ᎨᏒᎢ. (aiōnios g166)
Ndipo umboniwo ndi uwu: Mulungu anatipatsa moyo wosatha, ndipo moyowu uli mwa Mwana wake. (aiōnios g166)
12 ᎩᎶ ᎤᏁᎳᏅᎯ ᎤᏪᏥ ᎤᏪᎯ, ᎾᏍᎩ ᎬᏂᏛ ᎤᏪᎭ; ᎤᏁᎳᏅᎯᏃ ᎤᏪᏥ ᏄᏪᎲᎾ ᎥᏝ ᏳᏪᎭ ᎬᏂᏛ.
Iye amene ali ndi Mwana ali ndi moyo, amene alibe Mwana wa Mulungu alibe moyo.
13 ᎾᏍᎩ ᎯᎠ ᏄᏍᏗ ᎢᏨᏲᏪᎳᏏ ᎢᏦᎯᏳᎲᏍᎩ ᏚᏙᎥ ᎤᏁᎳᏅᎯ ᎤᏪᏥ, ᎢᏣᏙᎴᎰᎯᏍᏗᏱ ᎬᏂᏛ ᎢᏤᎲᎢ ᎨᏒᎢ, ᎠᎴ ᎢᏦᎯᏳᏗᏱ ᏚᏙᎥ ᎤᏁᎳᏅᎯ ᎤᏪᏥ. (aiōnios g166)
Ine ndikulemba zimenezi kwa inu, amene mwakhulupirira dzina la Mwana wa Mulungu kuti mudziwe kuti muli ndi moyo wosatha. (aiōnios g166)
14 ᎠᎴ ᎾᏍᎩ ᎯᎠ ᏄᏍᏗ ᎡᏙᎢᏳᏒᎢ, ᎾᏍᎩ ᎢᏳᏃ ᏂᎦᎥ ᎪᎱᏍᏗ ᎡᏗᏔᏲᏏ ᎣᏍᏛ ᎤᏰᎸᏗ ᎨᏒᎢ, ᎢᎦᏛᎦᏁᎲᎢ.
Ife timalimba mtima tikamafika pamaso pa Mulungu, popeza kuti ngati tipempha kanthu kalikonse monga mwa chifuniro chake, amatimvera.
15 ᎢᏳᏃ ᏱᏗᎦᏔᎭ ᎢᎦᏛᏁᎲᎢ, ᏂᎦᎥ ᎪᎱᏍᏗ ᎡᏗᏔᏲᏏ ᎢᏗᎦᏔᎰ ᎢᎩᏁᎲ ᎢᏳᏍᏗ ᎡᏗᏔᏲᏎᎸᎢ.
Ndipo ngati tikudziwa kuti amatimvera, chilichonse chimene timapempha, tikudziwanso kuti tili nacho chimene tamupempha Iye.
16 ᎢᏳᏃ ᎩᎶ ᏳᎪᎲ ᏗᎾᏓᏅᏟ ᏳᏍᎦᏅᏨ ᎠᏲᎱᎯᏍᏗ ᏂᎨᏒᎾ ᎠᏍᎦᏅᎢᏍᏗ ᎨᏒᎢ, ᎾᏍᎩ ᎠᏔᏲᎯᎮᏍᏗ ᎠᎴ ᎠᏎ ᎬᏂᏛ ᏓᏰᏥᏁᎵ ᎠᏲᎱᎯᏍᏗ ᏂᎨᏒᎾ ᎤᏂᏍᎦᏅᏨᎯ ᏅᏗᎦᎵᏍᏙᏗᏍᎬᎢ. ᎡᎭ ᎠᏍᎦᏅᎢᏍᏗ ᎠᏲᎱᎯᏍᏗ ᎨᏒᎢ, ᎥᏝ ᎠᏔᏲᎯᎮᏍᏗ ᎾᏍᎩ ᎠᏥᏙᎵᏍᏗᏱ ᏱᎦᏗᎭ.
Ngati wina aona mʼbale wake akuchita tchimo losadzetsa imfa, apemphere ndipo Mulungu adzamupatsa moyo mʼbale wakeyo. Ndikunena za ochita tchimo losadzetsa imfa. Pali tchimo lodzetsa imfa. Ine sindikunena kuti apemphere ayi.
17 ᏂᎦᎥ ᏚᏳᎪᏛ ᏂᎨᏒᎾ ᎾᏍᎩ ᎠᏍᎦᏂ, ᎡᎭᏃ ᎠᏍᎦᏅᎢᏍᏗ ᎨᏒ ᎠᏲᎱᎯᏍᏗ ᏂᎨᏒᎾ.
Chilichonse chosalungama ndi tchimo ndipo pali tchimo losadzetsa imfa.
18 ᎢᏗᎦᏔᎭ ᎩᎶ ᎤᏁᎳᏅᎯ ᎤᏕᏔᏅᎯ ᏥᎨᏐᎢ ᎥᏝ ᏯᏍᎦᏅᎪᎢ, ᎤᏁᎳᏅᎯᏍᎩᏂ ᎤᏕᏔᏅᎯ ᎤᎵᏍᏆᏂᎪᏙᎢ, ᎾᏍᎩᏃ Ꮎ ᎤᏁᎫᏥᏛ ᎥᏝ ᏳᏒᏂᎰᎢ.
Tikudziwa kuti aliyense amene ndi mwana wa Mulungu sachimwirachimwirabe. Yesu, Mwana wa Mulungu, amamusunga ndipo woyipa uja sangamukhudze.
19 ᎢᏗᎦᏔᎭ ᎤᏁᎳᏅᎯ ᏅᏓᎦᏓᎴᏅᎯ ᎨᏒᎢ, ᎠᎴ ᏂᎬᎾᏛ ᎡᎶᎯ ᎤᏃᏴᏨ ᎤᏲ ᎨᏒᎢ.
Tikudziwa kuti ndife ana a Mulungu ndi kuti dziko lonse lapansi lili pansi pa ulamuliro wa woyipayo.
20 ᎢᏗᎦᏔᎭᏃ ᎤᏁᎳᏅᎯ ᎤᏪᏥ ᎤᎷᏨᎢ, ᎠᎴ ᎢᎩᏁᎸ ᎢᎪᎵᏍᏗᏱ, ᎾᏍᎩ ᎡᏙᎵᏍᏗᏱ ᎾᏍᎩ ᎦᏰᎪᎩ ᏂᎨᏒᎾ ᏥᎩ; ᎠᎴ ᎾᏍᎩ ᎡᏗᏯᎠ ᎦᏰᎪᎩ ᏂᎨᏒᎾ ᏥᎩ, ᎾᏍᎩ ᎤᏪᏥ ᏥᏌ ᎦᎶᏁᏛ. ᎾᏍᎩ ᎯᎠ ᎤᏙᎯᏳᎯᏯ ᎤᏁᎳᏅᎯ, ᎠᎴ ᏫᎾᏍᏛᎾ ᎬᏂᏛ. (aiōnios g166)
Tikudziwa kuti Mwana wa Mulungu anafika ndipo anatipatsa nzeru, kuti timudziwe Iye amene ali woona. Ndipo ife tili mwa Iye amene ndi woona, Mwana wake, Yesu Khristu. Iye ndi Mulungu woona ndi moyo wosatha. (aiōnios g166)
21 ᏗᏥᏲᎵ, ᏕᏤᏯᏙᏤᎮᏍᏗ ᎤᏁᎳᏅᎯ ᏗᏰᎸᎯ. ᎡᎺᏅ.
Ana okondedwa, dzisungeni bwino, osapembedza mafano.

< ᏣᏂ ᎢᎬᏱᏱ ᎤᏬᏪᎳᏅᎯ 5 >