< 1 Korinthians 3 >

1 Ime miri vayi, me na tre niyi ni na ndi bi ruhu na ama nadi bi nema kpain bi mir ziza ni de kristi.
Ndipo abale sindikanakuyankhulani ngati auzimu koma adziko lapansi, makanda chabe mwa Khristu.
2 Me noyi mada ra ana hla wu sain mana, bina iri na kio zizan mal rina
Ndinakupatsani mkaka osati chakudya cholimba pakuti munali musanakonzeke kuchilandira. Zoonadi, simunakonzekebe.
3 Du zizan 'a bibi n'ma kpa, wa ingu ni do shishi he ni mi suron bi. Du naki bina to bina bi n'ma kpa na? Zirmbi wa indi ba tsra yi to?
Mukanali adziko lapansi. Pakuti pakati panu pali kaduka ndi kukangana, kodi si inu a dziko lapansi? Kodi simukuchita ngati anthu wamba?
4 Din iridi wa tre wawu “ni wu Bulus wawu ni kongon Afollos” naki bina ndi nlege na?
Pamene wina anena kuti, “Ine ndimatsatira Paulo,” ndipo wina akuti, “Ine ndimatsatira Apolo,” Kodi si inu akunja?
5 Me miya a nah Afollos? Anha Bulus? ana bi waba kuyir ni son mba, wabi kpaye ni ba nawa Irji noba du' na.
Ndiponso kodi Apolo ndi ndani? Nanga Paulo ndi ndani? Otumikira chabe, omwe kudzera mwa iwo inu munakhulupirira monga Ambuye anawagawira aliyense ntchito yake.
6 Ime me chu, u Apollos mba a bwa m'maa wu Rji a du ba Rju.
Ine ndinadzala mbewu, Apolo anayithirira, koma Mulungu ndiye anayikulitsa.
7 Naki iwa achu, ke niwa bwa m'ma ba na kpe na. Ama a hi Rji mba ni du gbro.
Choncho kuphatikiza iye wodzala ndi iye wothirira, onse sali kanthu, koma Mulungu yekha amene amakulitsa zinthu.
8 Wa achu niwa a bwa m'ma ba riri, u ko nha ani kpa knima tsra ni du wa a tei.
Munthu wodzala ndi munthu wothirira ali ndi cholinga chimodzi, ndipo aliyense adzapatsidwa mphotho molingana ndi ntchito yake.
9 Naki wawu mbu k'mir Rji kpukpambi duma wa ki zama ijhuma a tie ta.
Pakuti ife ndife antchito anzake a Mulungu; inu ndinu munda wa Mulungu, Nyumba ya Mulungu.
10 Ni alherin Rji wa ba ne, cikake wu meh wa meh zinci harsashi, uri ani meh ni whu me, du naki kowane indi aniya yada imeh ma ni he gyagyer.
Mwachisomo chimene Mulungu wandipatsa, ine ndinayika maziko monga mmisiri waluntha, ndipo ena akumangapo. Koma aliyense ayenera kuchenjera mmene akumangira.
11 Ba indi wa ni zinci harsashinma kan niwa ba riga da ziye wato Yesu Almasihu
Pakuti wina sangayikenso maziko ena oposera amene anakhazikitsidwa kale, amene ndi Yesu Khristu.
12 Zizan'a indi wa meh nitu har sashi rhi kan, wu zina riya ni wu ozurfa, koni wu titta bi daraja ni kukor, ni ciyawa ni tattaka.
Ngati munthu aliyense amanga pa maziko awa pogwiritsa ntchito golide, siliva, miyala yamtengowapatali, milimo yamitengo, tsekera kapena udzu,
13 du induma ni mlaye wa vyi wu mlaya ni he. Ani wu mlaya ni luwu. iluwu ni shell wu bima wa konha a teir.
ntchito yake idzaonekera pamene Tsiku la chiweruzo lidzazionetsa poyera. Tsikulo lidzafika ndi moto, ndipo motowo ndi umene udzayesa ntchito ya munthu aliyense.
14 Wu indiri wa duma abi, anika zizima.
Ngati zimene zamangidwazo sizidzagwa, adzalandira mphotho yake.
15 Toki wu indi wa induma a gonlu wawu aniyi da shaya asara u wawu ni tu ma ani nawo ama da kir.
Ndipo ngati zidzanyeke ndi moto, sadzalandira mphotho koma iye mwini adzapulumukabe, koma monga ngati munthu amene wapulumuka mʼmoto.
16 Binato di bi hai kadi u Rji u Ruhu Rji ani son ni kpambi na?
Kodi inu simukudziwa kuti ndinu Nyumba ya Mulungu ndipo kuti Mzimu wa Mulungu amakhala mwa inu?
17 Indi wa akpa haikali Rji u Ruhu Rji ti meme Irji game ni kpa ti meme. haikali Rji awu tsraki wukitaa me anaki.
Ngati wina aliyense awononga Nyumba ya Mulunguyo, Mulungu nayenso adzamuwononga ameneyo; popeza Nyumba ya Mulungu ndi yopatulika ndipo Nyumbayo ndi inu amene.
18 Du ndio duna gur tuma n, idi wa aya tuma ani wawu kpe, ni son bi wawu, waniya ni wawu a zan konha, di wawu a he ni hikima niton mbu wu zizan du k'ma ti wawu don da zama u hikima. (aiōn g165)
Choncho musadzinyenge. Ngati wina wa inu akuganiza kuti ndi wanzeru pa mulingo wa mʼbado uno, ayenera kukhala “wopusa” kuti athe kukhala wanzeru. (aiōn g165)
19 U hikima wu gbugbu'u yi kalacu mu ni Rji naki itre ma ba hna da tre “ani vuu bi hikima ni makircin mba.”
Pakuti nzeru ya dziko lapansi ndi yopusa pamaso pa Mulungu. Monga kwalembedwera kuti, “Iye amakola anthu ochenjera mu msampha wa kuchenjera kwawo,”
20 Har luwa 'Irji to mer bi hikima a wu megye”.
ndiponso, “Ambuye amadziwa kuti maganizo a wanzeru ndi opandapake.”
21 Tok ni meryi du ndio du na wur who ni indi na duka koge hi wume.
Choncho, wina asanyadire anthu chabe! Zonse ndi zanu,
22 Ni Bulus u Apollos, U kefas, u gbu-gblu u rai, u que u kpi wu zizan, u kpi bi ye no ko shishi, wawu ba wu mbi.
kaya Paulo kapena Apolo kapena Kefa kapena dziko lapansi, kapena moyo, kapena imfa, kapena tsopano, kapena mʼtsogolo, zonse ndi zanu,
23 U biyi biwu kristi, u kristi hi wu Rji
ndipo inu ndinu a Khristu, ndipo Khristu ndi wa Mulungu.

< 1 Korinthians 3 >