< Titus 2 >

1 Bara nani febele ilemon iyina nin ti pipin ticine.
Koma iwe uziphunzitsa zogwirizana ndi chiphunzitso choona.
2 Anit akune suu anan kifuu batiitikune anan yenju upi, uyinu sa uyenua anan suu, nin nanan ciu nayi.
Phunzitsa amuna achikulire kuti akhale osaledzera, aulemu wawo, odziletsa, okhwima mʼchikhulupiriro, mʼchikondi ndi mʼkupirira.
3 Awani akune inin wang nanere iso anan nakpinati, na anan kubelin ba. Naniwa suu acin kitin nssu turo b. Na idursuzo ilemong na idi gigime
Chimodzimodzinso, phunzitsa amayi achikulire kuti akhale aulemu mʼmakhalidwe awo, asakhale osinjirira anzawo kapena zidakwa, koma akhale alangizi abwino.
4 bara ina taa awni abebene isu dert nanya kpilzu mer, iti nani likara nibinai iti usuu nales mine nang nono isoo anang yeju ipiit.
Tsono atha kulangiza amayi achichepere kukonda amuna awo ndi ana awo.
5 Nlau anang lisosin licine ndarrti isau anan nanku nati nin nales mine bara uliru Kutelle wa so imong infillu
Kuwaphunzitsa kukhala odziletsa ndi oyera mtima, osamala bwino mabanja awo, okoma mtima, ndi ogonjera amuna awo. Choncho palibe amene adzanyoze mawu a Mulungu.
6 Nanere tutung beleng azamane iso anan kpilzunupiit.
Momwemonso, uwalimbikitse amuna achichepere kuti akhale odziletsa.
7 nanya nimong vat durum atee mine nafo anan katwa ka cine; iwa dursuzu durung nlau durung tikune, nin tigbulang tine tin salin yenu.
Pa zonse iwe mwini ukhale chitsanzo pa ntchito zabwino. Pa chiphunzitso chako uwonetsa kuona mtima ndi kutsimikiza mtima kwako.
8 Belen pipinghe tuu na ti na so sa ukye, bara tina soo nin cin kitene nle na aba tifi mayarda, bara nani na imenmun inanzan duku na iba benlu nati bite ba.
Phunzitsa choonadi kuti anthu asapeze chokutsutsa, motero wotsutsana nawe adzachita manyazi chifukwa adzasowa kanthu koyipa kuti atinenere.
9 Acin ba suu unaku nati kit nacinilarimine idertin inan poo nani nibina, na iwa sa mayardan nan ghinu ba.
Phunzitsa akapolo kuti azigonjera ambuye awo mu zinthu zonse ndi kuwakondweretsa. Asamatsutsane nawo
10 Na iwa su nani likiri b, bara nani na idursu nni uyinu sa uyen, bara inan taa udursuzu bite mbelen Kutelle unan tucu bite kuna niyizi nanya tibau vat.
kapena kumawabera, koma adzionetse kuti ndi odalirika, motero pa zochita zawo zonse adzaonetsa ubwino wa chiphunzitso cha Mulungu, Mpulumutsi wathu.
11 Iyen, ubolu Kutelle na uma dak nin tucu udu nanit vat.
Pakuti chisomo cha Mulungu chimene chimapulumutsa chaonekera kwa anthu onse.
12 Unin dursuzu nani ti nari imon inanzang nin kunanizi nimun iyi ti suu anan kujijin, anit alau nin libau Kutelle nanya ku kuje. (aiōn g165)
Chisomo chimatiphunzitsa kukana moyo osalemekeza Mulungu komanso zilakolako za dziko lapansi. Ndipo chimatiphunzitsa kukhala moyo odziletsa, olungama ndi opembedza Mulungu nthawi ino, (aiōn g165)
13 Na ti din ncaa ti saru nin nayi aboo dak ngongon udiya Kutelle bit nin Yesu Kristi unan tucu.
pamene tikudikira chiyembekezo chodala; kuonekera kwa ulemerero wa Mulungu wathu wamkulu ndi Mpulumutsi, Yesu Khristu,
14 Yesu wa ni liti mee bara arik tinan se ulau kusain nuzu na lapibit tinin soo lau kitime, alena a ceu nibinai nsu nimon icine
amene anadzipereka yekha chifukwa cha ife kutiwombola ku zoyipa zonse ndi kudziyeretsera yekha anthu amene ndi akeake, achangu pa ntchito yabwino.
15 Beleng ni likara kibinai ni le mone nin te nke nin tigoo vat na imong wa nari minu ba.
Tsono zimenezi ndi zinthu zomwe uyenera kuphunzitsa. Uziwalimbikitsa anthu ndi kuwatsutsa komwe. Uzichita zimenezi ndi ulamuliro wonse. Wina aliyense asakupeputse ayi.

< Titus 2 >